Loading...

Download
  • Genre:Soul
  • Year of Release:2022

Lyrics

M'ma

Makadidi


Abusa mpepheleniko

Muli matenda mthupimo

Nsanje yalowa mkatimo

Abusa mpempheleniko

Ndine mfana oyimba bho

Koma ndimadana ndi anzanga oyimba kuposa ineyo

Oblowa kuposa ineyo

Chifukwa amayimba lokolo

Abusa mpempheleniko

Ndimafuna nditakhala wabwino

Koma zimangovuta mkatimo


Abusa mpempheleniko

Muli ziwanda mthupimo

Zinabwela ndi dollar zo

Abusa mpepheleniko

Ndine mfana wochita bho

Ndilinso ndi chi nkazi chabwino

Abusa mpempheleniko

Ndakosoneza banja lo

Langa ndi mzanga wabwino

Abusa mpempheleniko

Ndimafuna nditakhala wabwino

Koma zimangovuta mkatimo


Muli nkhondo muli nkhondo

Makadidido ali pa moto

Ndi chitonzo ndi chitonzo

Kukhala ochita bwino kumaloto kokha

Nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo


Muli nkhondo mumtima

Ndili mumdima

Kuwala mmoyo mwanga kunazima

Kuwona ndimafuna maso anafa

Kufunitsitsa ndiye ndimafuna

Ndisiye kuzunza akazi angawa

Ndisiye kuzunza ana angawa

Ndisiye kuzunza ana amasiye

Ndisiye kubela anthu osauka

Ndimafuna nditasintha

Ndisiye kuzunguza anthu mu ghetto mwathu akumandidandaula

Ndufuna nditasintha

Ngati sukulu sindingamangile anawa ndinalowelanji m'boma

Oh my God oh my God

Abusa mundipempheleleko

Pachuluka chinyengo pa dziko

Abusa mundipempheleleko


Muli nkhondo muli nkhondo

Makadidido ali pa moto

Ndi chitonzo ndi chitonzo

Kukhala ochita bwino kumaloto kokha

Nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo


GD sewa sewa

Atate woyera Yehova wamakamu, bless

Tabwela pamaso pano ndi mwana wanu, yes

Ali ndi nkhondo mu mtima mpatseni mdalitso

Ndi ochimwa koma amafuna mparadizo

Wachimasomaso kuponya ponya diso

Ali ndi zofooka akupempha chilimbikitso

Luka 4 verse 2 yesu anayesedwa

Yang'ana Yobu chapter 1 yobu anayesedwa

Genesis 39 Yosefe anayesedwa

Chi khristu ndi nkhondo ndipo tonsefe tidzayesedwa

Satana ndi mzimu sungamuphe ndi nkondo

Nkhodo ya uzimu timamenya pa mawondo

Zimatheka kutopa Mose anakwezedwa nkono

Khala ochilimika osamangoliza nkono no no

No it's a battle for the soul

The devil creeping on a low victory is slow

We gon' win it with every blow

Imatelo nkhondo ya mu mtimamo


Muli nkhondo muli nkhondo

Makadidido ali pa moto

Ndi chitonzo ndi chitonzo

Kukhala ochita bwino kumaloto kokha

Nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo

Muli nkhondo

Similar Songs

+

      -   or   -

      -   or   -

      NG +234

          Please Select A Playlist

          Add New Playlist

          Share on

          Embed: Love & Light EP

          Custom Size :

          • Default
          • Desktop(300*600)
          • Mobile(300*250)

          Type :

          • HTML/HTML5 (WordPress Supported)
          Get Boomplay Premium
          for
          Payment Method
          Pay With
            Review and pay
            Order Date
            Payment Method
            Due Today
            Flutterwave
              Subscription Successful

              Congratulations! You have successfully activated Boomplay 1 Month Premium.

              Now you have access to all the features of Boomplay App.
              Payment Failed

              Please check your balance and then try again.

              You'll lose your subscription if we don't have a working payment method for your account, so please check your payment details.
              Need help? Contact Boomplay Subscription Support.
              Payment Processing...
              10 s

              Payment is being processed by . Please wait while the order is being comfirmed.

              Payment Processing
              Your order is processing, and it may take up to a few days for the service provider to handle your payment. Please kindly stay tuned and check your order status in ‘User Center’.
              About Order Status